Genesis 9:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsopano mubalane, kuti zidzukulu zanu zidzachulukane ndi kudzabalalika pa dziko lonse lapansi.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndi inu, mubalane, muchuluke; muswane pa dziko lapansi, nimuchuluke m'menemo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Inu muberekane ndi kuchulukana kuti mudzaze dziko lonse lapansi ndi kuligonjetsa.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndi inu, mubalane, mucuruke; muswane pa dziko lapansi, nimucuruke m'menemo.