Habakkuk 1:14 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mumasandutsa anthu kuti azikhala ngati nsomba zam'nyanja, ngati zokwaŵa zimene zilibe wozilamulira?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndi kuyesa anthu ngati nsomba za m'nyanja, ngati zokwawa zopanda wakuzilamulira.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mwasandutsa anthu kukhala ngati nsomba zamʼnyanja, ngati zolengedwa zamʼnyanja zimene zilibe wolamulira.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndi kuyesa anthu ngati nsomba za m'nyanja, ngati zokwawa zopanda wakuzilamulira.