Habakkuk 2:7 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Angongolewo adzakuukira mwadzidzidzi. Adzakuchititsa mantha ndi kukulanda zako zonse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Sadzauka kodi modzidzimuka iwo amene adzakuluma, ndi kugalamuka iwo amene adzakugwedezetsa; ndipo udzakhala zofunkha zao?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi angongole ako sadzakuwukira mwadzidzidzi? Kodi sadzadzuka ndi kukuchititsa mantha? Pamenepo iwe udzalandidwa kalikonse.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Sadzauka kodi modzidzimuka iwo amene adzakuluma, ndi kugalamuka iwo amene adzakugwedezetsa; ndipo udzakhala zofunkha zao?