Haggai 1:10 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nkuwonatu mvula yati zii, nthaka yati gwa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
M'mwemo chifukwa cha inu kumwamba kukaniza mame, ndi nthaka ikaniza zipatso zake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Choncho, chifukwa cha inu, mitambo yaleka kugwetsa mvula ndipo dziko lapansi laleka kutulutsa zomera.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
M'mwemo cifukwa ca inu kumwamba kukaniza mame, ndi nthaka ikaniza zipatso zace.