Haggai 1:3 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono Chauta adapatsa mneneri Hagai uthenga uwu wakuti:
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pamenepo mau a Yehova anadza mwa Hagai mneneri, ndi kuti,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsono Yehova anayankhula ndi mneneri Hagai kuti,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pamenepo mau a Yehova anadza mwa Hagai mneneri, ndi kuti,