Haggai 1:4 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Kodi nzabwino zimenezi kuti inuyo muzikhala m'nyumba zomanga bwino, pamene Nyumba yangayi ili bwinja?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kodi imeneyi ndiyo nthawi yakuti inu nokha mukhala m'nyumba zanu zochingidwa m'katimo, ndi nyumba iyi ikhale yopasuka?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Kodi ino ndi nthawi yoti inuyo muzikhala mʼnyumba zomanga bwino, pamene Nyumba yangayi ikanali bwinja?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kodi imeneyi ndiyo nthawi yakuti inu nokha mukhala m'nyumba zanu zocingidwa m'katimo, ndi nyumba iyi ikhale yopasuka?