Haggai 1:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Nchifukwa chake tsono Ine Chauta Wamphamvuzonse ndikunena kuti muganizepo bwinotu pamenepa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chifukwa chake tsono, atero Yehova wa makamu: Mtima wanu usamalire njira zanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsono zimene Yehova Wamphamvuzonse akunena ndi izi, “Ganizirani bwino njira zanu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cifukwa cace tsono, atero Yehova wa makamu: Mtima wanu usamalire njira zanu.