Haggai 1:8 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kwerani ku mapiri, mukadule nsichi, mudzandimangire Nyumba yoyenera, kuti ndikondwere nayo ndi kulandiriramo ulemerero.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kwerani kudziko la mapiri, ndi kukwera nayo mitengo, nimumange nyumbayi; ndipo kudzandikomera, ndipo ndidzalemekezedwa, ati Yehova.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pitani ku mapiri ndipo mukatenge matabwa oti mudzamangire Nyumba yanga, kuti ndikondwere nayo ndi kulandiramo ulemu,” akutero Yehova.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kwerani ku dziko la mapiri, ndi kukwera nayo mitengo, nimumange nyumbayi; ndipo kudzandikomera, ndipo ndidzalemekezedwa, ati Yehova.