Hebrews 1:14 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nanga angelo, kodi suja iwo ndi mizimu yotumikira chabe, imene Mulungu amaituma chifukwa cha anthu odzalandira chipulumutso?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kodi siili yonse mizimu yotumikira, yotumidwa kuti itumikire iwo amene adzalowa chipulumutso?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi angelo onse si mizimu yotumikira odzalandira chipulumutso?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kodi siiri yonse mizimu yotumikira, yotumidwa kuti itumikire iwo amene adzalowa cipulumutso?