Hebrews 1:4 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mwana wa Mulunguyo ngwoposa angelo, monga momwe dzina limene Mulungu adampatsa limaposera dzina la angelo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
atakhala wakuposa angelo, monga momwe adalowa dzina lakuposa iwo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mwanayu ndi wamkulu koposa angelo, monga momwe dzina limene analandira limaposa dzina la angelo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
atakhala wakuposa angelo, monga momwe adalowa dzina lakuposa iwo.