Hebrews 13:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tiyeni tsono tilimbe mtima ndi kunena kuti, “Ambuye ndiwo Mthandizi wanga, sindidzachita mantha. Munthu angandichite chiyani?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kotero kuti tinena molimbika mtima, Mthandizi wanga ndiye Ambuye; sindidzaopa; adzandichitira chiyani munthu?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kotero ife tikunena molimba mtima kuti, “Ambuye ndiye mthandizi wanga; sindidzachita mantha. Munthu angandichitenji ine?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kotero kuti tinena molimbika mtima, Mthandizi wanga ndiye Ambuye; smdidzaopa; Adzandicitira ciani munthu?