Hebrews 2:16 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Paja nchodziŵikiratu kuti sadatekeseke ndi angelo ai koma ndi zidzukulu za Abrahamu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti ndithu salandira angelo, koma alandira mbeu ya Abrahamu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pakuti tikudziwanso kuti sathandiza angelo, koma zidzukulu za Abrahamu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti ndithu salandira angelo, koma alandira mbeu ya Abrahamu.