Hebrews 3:15 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Paja Malembo akuti, “Lero lino mukamva mau a Mulungu, musaumitse mitima yanu monga muja zidaachitikira poukira Mulungu.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
umo anenamo, Lero ngati mudzamva mau ake, musaumitse mitima yanu, monga pa kupsetsa mtima.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Monga kunanenedwa kuti, “Lero ngati mumva mawu ake, musawumitse mitima yanu ngati momwe munachitira pamene munawukira.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
umo anenamo, Lero ngati mudzamva mau ace, Musaumitse mitima yanu, monga pa kupsetsa mtima.