Hebrews 3:18 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nanga Mulungu ankanena za yani pamene adaati, “Ndikulumbira kuti ameneŵa sadzaloŵa konse mu mpumulo umene ndidaŵakonzera?” Pajatu ankanena za anthu amene adaamuukira.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo adawalumbirira ayani kuti asalowe mpumulo wake?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nanga Mulungu ankanena za ndani kuti sadzalowa mu mpumulo wake? Pajatu ankanena za anthu amene sanamvere aja.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo adawalumbirira ayani kuti asalowe mpumulo wace?