Hebrews 3:2 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Paja Iye anali wokhulupirika kwa Mulungu amene adampatsa udindowo, monga momwe Mosenso anali wokhulupirika m'nyumba yonse ya Mulungu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
amene anakhala wokhulupirika kwa Iye adamuikayo, monganso Mose m'nyumba yake yonse.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye anali wokhulupirika kwa Mulungu amene anamupatsa udindowo, monga momwe Mose anali wokhulupirika mʼnyumba yonse ya Mulungu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
amene anakhala wokhulupirika kwa iye adamuikayo, monganso Mose m'nyumba yace yonse.