Hebrews 3:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nchifukwa chake tsono, monga Mzimu Woyera akunenera, “Lero lino mukamva mau a Mulungu,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Momwemo, monga anena Mzimu Woyera, Lero ngati mudzamva mau ake,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsono monga Mzimu Woyera akuti, “Lero mukamva mawu ake,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Momwemo, monga anena Mzimu Woyera, Lero ngati mudzamva mau ace,