Hebrews 3:8 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
musaumitse mitima yanu monga muja zidaachitikira pomuukira Mulungu, tsiku la kumuyesa m'chipululu muja.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
musaumitse mitima yanu, monga m'kupsetsa mtimamo, monga muja tsiku la chiyesero m'chipululu,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
musawumitse mitima yanu ngati munachitira pamene munawukira, pa nthawi yoyesedwa mʼchipululu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Musaumitse mitima yanu, monga m'kupsetsa mtimamo, Monga muja tsiku la ciyesero m'cipululu,