Hebrews 5:8 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Motero Yesu, ngakhale anali Mwana wa Mulungu, adaphunzira kumvera pakumva zoŵaŵa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
angakhale anali Mwana, anaphunzira kumvera ndi izi adamva kuwawa nazo;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngakhale Iye anali Mwana wa Mulungu anaphunzira kumvera pomva zowawa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
angakhale anali Mwana, anaphunzira kumvera ndi izi adamva kuwawa nazo;