Hebrews 7:22 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kusiyana kokhudza lumbiroku kukutiwonetsa kuti Yesu ndi Nkhoswe yotsimikizira Chipangano choposa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Momwemonso Yesu wakhala Nkhoswe ya pangano loposa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Chifukwa cha lumbiroli, Yesu wakhala Nkhoswe ya Pangano lopambana.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Momwemonso Yesu wakhala Nkhoswe ya pangano loposa.