Hosea 1:8 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Sakondedwa ataleka kuyamwa, Gomeri adatenganso pena pathupi, nabala mwana winanso wamwamuna.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ataleka tsono kuyamwitsa Wosachitidwa-chifundo, anaima, nabala mwana wamwamuna.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Sakondedwa ataleka kuyamwa, Gomeri anabereka mwana wina wamwamuna.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ataleka tsono kuyamwitsa Wosacitidwa cifundo, anaima, nabala mwana wamwamuna.