Hosea 10:4 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mafumu akungolankhula mau opandapake. Amangochita zipangano ndi malonjezo abodza. Chilungamo chasanduka kusalungama kumene kumaphuka ngati udzu woipa m'munda.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Anena mau akulumbira monama, pakuchita mapangano momwemo; chiweruzo chiphuka ngati zitsamba zowawa m'michera ya munda.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mafumu amalonjeza zambiri, amalumbira zabodza pochita mapangano. Kotero maweruzo amaphuka ngati zitsamba zakupha mʼmunda umene walimidwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Anena mau akulumbira monama, pakucita mapangano momwemo; ciweruzo ciphuka ngati zitsamba zowawa m'micera ya munda.