Hosea 10:6 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Zoonadi, fanolo lidzatengedwa kupita ku Asiriya, kuti likakhale mphatso yoperekedwa kwa mfumu yaikulu. Aefuremu adzachita manyazi, Aisraelewo adzachita manyazi chifukwa cha malangizo onama amene ankamvera.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Adzachitengeranso ku Asiriya chikhale mphatso ya kwa mfumu Yarebu; Efuremu adzatenga manyazi, ndi Israele adzachita manyazi ndi uphungu wake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Fanolo lidzatengedwa kupita ku Asiriya ngati mphatso kwa mfumu yayikulu. Efereimu adzachititsidwa manyazi chifukwa cha mafano ake amitengo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Adzacitengeranso ku Asuri cikhale mphatso ya kwa mfumu Yarebu; Efraimu adzatenga manyazi, ndi Israyeli adzacita manyazi ndi uphungu wace.