Hosea 10:9 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chauta akuti, “Kuyambira uchimo wa ku Gibea, Aisraele akhala akuchimwabe. Motero adzagonjetsedwa pa nkhondo ku Gibea komweko.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Israele, wachimwa kuyambira masiku a Gibea; pomwepo anaimabe; nkhondo ya ana a chosalungama siinawapeza ku Gibea.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Iwe Israeli, wachimwa kuyambira mʼmasiku a Gibeya, ndipo wakhala uli pomwepo. Kodi nkhondo sinagonjetse anthu ochita zoyipa ku Gibeya?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Israyeli, wacimwa kuyambira masiku a Gibeya; pomwepo anaimabe; nkhondo ya pa ana a cosalungama siinawapeza ku Gibeya.