Hosea 11:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Tsono anthuwo adzabwereranso ku ukapolo ku Ejipito. Aasiriya adzakhala oŵalamulira, pakuti iwo akana kubwerera kwa Ine.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Iye sadzabwerera kunka kudziko la Ejipito, koma Asiriya adzakhala mfumu yake, popeza anakana kubwera.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Sadzabwerera ku Igupto, koma Asiriya ndiye adzakhala mfumu yawo pakuti akana kutembenuka.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Iye sadzabwerera kumka ku dziko la Aigupto, koma Asuri adzakhala mfumu yace, popeza anakana kubwera.