Hosea 12:2 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chauta akuŵaimba mlandu anthu a ku Yuda. Adzalanga a m'banja la Yakobe chifukwa cha makhalidwe ao, adzaŵabwezera zolingana ndi ntchito zao zoipa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Yehova ali ndi mlandu ndi Yuda, nadzalanga Yakobo monga mwa njira zake, adzambwezera monga mwa machitidwe ake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yehova akuyimba mlandu Yuda; Iye adzalanga Yakobo molingana ndi makhalidwe ake, adzamulanga molingana ndi ntchito zake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Yehova ali ndi mlandu ndi Yuda, nadzalanga Yakobo monga mwa njira zace, adzambwezera monga mwa macitidwe ace.