Hosea 13:11 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndidakupatsani mafumu mwachipsera mtima. Kenaka atandikwiyitsa, ndidaŵachotsa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndinakupatsa mfumu mu mkwiyo wanga; ndinamchotsanso m'ukali wanga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Choncho Ine ndinakupatsani mfumu mwachipseramtima, ndipo ndinayichotsa mwaukali.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndinakupatsa mfumu mu mkwiyo wanga; ndinamcotsanso m'ukali wanga.