Hosea 13:12 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Kuipa kwa anthu a ku Efuremu kwalembedwa m'buku, buku lake la machimo ao ndalisunga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mphulupulu ya Efuremu yamangika, tchimo lake lisungika.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kulakwa kwa Efereimu kwasungidwa, machimo ake alembedwa mʼbuku.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mphulupulu ya Efraimu yamangika, cimo lace lisungika.