Hosea 13:6 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndidaŵadyetsa, nakhuta, koma atakhuta, adanyada, ndipo adandiiŵala Ine.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Monga mwa podyetsa pao, momwemo anakhuta; anakhuta, ndi mtima wao unakwezeka; chifukwa chake anandiiwala Ine.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pamene ndinawadyetsa, iwo anakhuta; iwo atakhuta anayamba kunyada; ndipo anandiyiwala Ine.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Monga mwa podyetsa pao, momwemo anakhuta; anakhuta, ndi mtima wao unakwezeka; cifukwa cace anandiiwala Ine.