Hosea 13:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Motero ndidzaŵalumphira ngati mkango, ndidzaŵalalira ngati kambuku m'mbali mwa njira.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chifukwa chake ndikhala nao ngati mkango; ngati nyalugwe ndidzalalira kunjira.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Motero ndidzawalumphira ngati mkango, ndidzawabisalira mu msewu ngati kambuku.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cifukwa cace ndikhala nao ngati mkango; ngati nyalugwe ndidzalalira kunjira.