Hosea 14:3 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Aasiriya sadzatipulumutsa, akavalo ankhondo sadzatiteteza. Chimene tidapanga ndi manja athu sitidzachitchulanso kuti, ‘Mulungu wathu,’ pakuti ndinu amene mumachitira chifundo amasiye.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Asiriya sadzatipulumutsa; sitidzayenda pa akavalo, ndipo sitidzanenanso kwa ntchito ya manja athu, Inu ndinu milungu yathu; pakuti mwa Inu ana amasiye apeza chifundo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Asiriya sangatipulumutse; ife sitidzakwera pa akavalo ankhondo, sitidzanenanso kuti, ‘Milungu yathu’ kwa zimene manja athu omwe anazipanga, pakuti ndinu amene mumachitira chifundo ana amasiye.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Asuri sadzatipulumutsa; sitidzayenda pa akavalo, ndipo sitil dzanenanso kwa nchito ya manja athu, Inu ndinu milungu yathu; pakuti mwa Inu ana amasiye apeza cifundo.