Hosea 6:11 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Inunso Ayuda mudzakolola chilango.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Akuikidwiratunso nyengo yakukolola, Yuda iwe, pamene ndikabwezanso undende wa anthu anga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Kunenanso za iwe Yuda, udzakolola chilango. “Pamene ndiwabwezere anthu anga zinthu zabwino.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Akuikidwiratunso nyengo yakukolola, Yuda iwe, pamene ndikabwezanso undende wa anthu anga.