Hosea 7:12 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kulikonse kumene amapita, ndidzaŵatchera ukonde. Ndidzaŵagwetsa pansi ngati mbalame zamumlengalenga. Ndidzaŵalanga chifukwa cha zolakwa zao.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pamene amuka ndidzawayalira ukonde wanga, ndidzawagwetsa ngati mbalame za m'mlengalenga, ndidzawalanga monga udamva msonkhano wao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Akamadzapita, ndidzawakola ndi ukonde wanga; ndidzawagwetsa pansi ngati mbalame zamumlengalenga. Ndikadzamva kuti asonkhana pamodzi ndidzawakola.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pamene amuka ndidzawayalira ukonde wanga, ndidzawagwetsa ngati mbalame za m'mlengalenga, ndidzawalanga monga udamva msonkhano wao.