Hosea 7:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mitima yao imatentha ngati uvuni ndi upo wao. Usiku wonse, ukali wao umanyeka, ndipo m'maŵa umayaka ngati moto.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti asendera nao mtima wao wakunga ng'anjo ya mkate, pokhala alikulalira; woocha mkate wao agona usiku wonse, m'mawa iyaka ngati moto wa malawi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mitima yawo ili ngati uvuni; amayandikira Mulungu mwachiwembu. Ukali wawo umanyeka usiku wonse, mmawa umayaka ngati malawi a moto.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti asendera nao mtima wao wakunga ng'anjo ya mkate, pokhala alikulalira; wooca mkate wao agona usiku wonse, m'mawa iyaka ngati moto wa malawi.