Hosea 8:1 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chauta akuti, “Lizani lipenga! Adani akugudukira dziko la Chauta ngati adembo pamwamba pa nyama. Anthu anga aphwanya chipangano changa, ndipo achimwira malamulo anga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Lipenga kukamwa kwako. Akudza ngati chiombankhanga, kulimbana ndi nyumba ya Yehova; chifukwa analakwira chipangano changa, napikisana nacho chilamulo changa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Ika lipenga pakamwa pako. Ngati chiwombankhanga, kutsutsana ndi nyumba ya Yehova chifukwa anthu aphwanya pangano langa ndiponso agalukira lamulo langa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Lipenga kukamwa kwako, Akudza ngati ciombankhanga, kulim bana ndi nyumba ya Yehova; cifukwa analakwira cipangano canga, napikisana naco cilamulo canga.