Hosea 8:10 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chifukwa choti adagwirizana ndi anthu a mitundu ina, ndidzaŵasonkhanitsa ndi kuŵaononga. Posachedwa adzazunzika kwambiri chifukwa cha ulamuliro wa mfumu ya ku Asiriya.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Inde angakhale alembera mwa amitundu ndidzawasonkhanitsa tsopano; ndipo ayamba kuchepa chifukwa cha katundu wa mfumu ya akalonga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngakhale wadzigulitsa pakati pa mitundu ya anthu, Ine ndidzawasonkhanitsa pamodzi. Iwo adzayamba kuzunzika pansi pa ulamuliro wankhanza wa mfumu yamphamvu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Inde angakhale alembera mwa amitundu ndidzawasonkhanitsa tsopano; ndipo ayamba kucepa cifukwa ca katundu wa mfumu ya akalonga.