Hosea 8:2 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Amalirira kwa Ine kuti ndiŵathandize, amati, ‘Ife Aisraele tikukudziŵani Inu Mulungu wathu.’
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Adzafuulira kwa Ine, Mulungu wanga, ife Aisraele tikudziwani.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Israeli akulirira kwa Ine kuti, ‘Inu Mulungu wathu, ife timakudziwani!’
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Adzapfuulira kwa Ine, Mulungu wanga, ife Aisrayeli tikudziwani.