Hosea 9:11 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ulemerero wa Aefuremu udzaŵathaŵa mouluka ngati mbalame. Sadzabalanso ana. Akazi ao sadzaima, sadzatenga pathupi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kunena za Efuremu, ulemerero wao udzauluka ndi kuchoka ngati mbalame; sipadzakhala kubala, ndi kukhala ndi pakati, ndi kuima.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ulemerero wa Efereimu udzawuluka ngati mbalame. Sipadzakhalanso kubereka ana, kuyembekezera kapena kutenga pathupi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kunena za Efraimu, ulemerero wao udzauluka ndi kucoka ngati mbalame; sipadzakhala kubala, ndi kukhala ndi pakati, ndi kuima.