Hosea 9:12 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ngakhale abale ana, ndidzaŵaononga, sadzakhalapo ndi mmodzi yemwe. Tsoka kwa anthuwo ndikadzaŵasiya.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Angakhale alera ana ao, koma ndidzawasowetsa, wosatsala munthu; ndithunso tsoka iwowa, pamene ndiwachokera.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngakhale atalera ana ndidzachititsa kuti mwana aliyense amwalire. Tsoka kwa anthuwo pamene Ine ndidzawafulatira!
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Angakhale alera ana ao, koma ndidzawasowetsa, wosatsala munthu; ndithunso tsoka iwowa, pamene ndiwacokera.