Hosea 9:13 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Inu Chauta, monga ndikuwonera, ana a Efuremu adzakhala ngati nyama zojiwa. Aefuremu adzatsogolera ana ao kunkhondo kumene adzaphedwe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Efuremu, monga ndaona, akunga Tiro, wookedwa pokoma; koma Efuremu adzatulutsira ana ake wakuwaphera.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndaona Efereimu ngati Turo, atadzalidwa pa nthaka ya chonde. Koma Efereimu adzatsogolera ana ake kuti akaphedwe.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Efraimu, monga ndaona, akunga Turo, wookedwa pokoma; koma Efraimu adzaturutsira ana ace wakuwaphera.