Hosea 9:16 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Efuremu ali ngati mtengo wodulidwa umene mizu yake yauma, ndipo sudzabalanso zipatso. Ngakhale anthuwo abale ana, ndidzaŵapha ana ao okondedwawo.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Efuremu wakanthidwa, muzu wao wauma, iwo sadzabala zipatso; inde ngakhale abala, koma ndidzapha zipatso zofunika za mimba yao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Efereimu wathedwa, mizu yake yauma sakubalanso zipatso. Ngakhale atabereka ana, Ine ndidzapha ana awo okondedwawo.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Efraimu wakanthidwa, muzu wao wauma, iwo sadzabala zipatso; inde ngakhale abala, koma ndidzapha zipatso zofunika za mimba yao.