Hosea 9:17 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mulungu wanga adzaŵataya anthu amenewo chifukwa choti sadamumvere. Adzasanduka oyendayenda pakati pa mitundu ya pa dziko lapansi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mulungu wanga adzawataya, pakuti sanammvere Iye; ndipo adzakhala othawathawa mwa amitundu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mulungu wanga adzawakana chifukwa sanamumvere Iye; adzakhala oyendayenda pakati pa anthu a mitundu ina.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mulungu wanga adzawataya, pakuti sanammvera Iye; ndipo adzakhala othawathawa mwa amitundu.