Isaiah 1:19 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ngati muli okonzeka kundimvera, mudzalidyera dziko.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ngati inu muli ofuna ndi omvera, mudzadya zabwino za dziko,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngati muli okonzeka kundimvera mudzadya zinthu zabwino za mʼdziko;
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ngati inu muli ofuna ndi omvera, mudzadya zabwino za dziko,