Isaiah 1:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kuchokera kuphazi mpaka kumutu palibe pabwino, ponse pali mikwingwirima ndi zilonda, mabala ali magazi chuchuchu. Mabala ake ngosatsuka, ngosamanga, ndiponso ngosapaka mafuta ofeŵetsa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kuchokera pansi pa phazi kufikira kumutu m'menemo mulibe changwiro; koma mabala, ndi mikwingwirima, ndi zilonda; sizinapole, ngakhale kumangidwa, ngakhale kupakidwa mafuta.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kuchokera ku phazi mpaka ku mutu palibe pabwino, paliponse pali mikwingwirima ndi zilonda, mabala ali magazi chuchuchu, mabala ake ngosatsuka, ngosamanga ndiponso ngosapaka mafuta ofewetsa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kucokera pansi pa phazi kufikira kumutu m'menemo mulibe cangwiro; koma mabala, ndi mikwingwirima, ndi zironda; sizinapole, ngakhale kumangidwa, ngakhale kupakidwa mafuta.