Isaiah 10:21 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Otsalira adzabwerera, otsalira a m'banja la Yakobe, adzabwereradi kwa Mulungu wamphamvu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Otsala adzabwera, otsala a Yakobo, kwa Mulungu wamphamvu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Otsalira adzabwerera, otsalira a Yakobo adzabwerera kwa Mulungu Wamphamvu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Otsala adzabwera, otsala a Yakobo, kwa Mulungu wamphamvu.