Isaiah 10:25 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Patsala pang'onong'ono kuti uthe mkwiyo wanga pa inu, koma ndidzaŵakwiyira iwonso mpaka kuŵaononga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti patsala kamphindi, ndipo ukali udzathedwa ndi mkwiyo wanga wakuwaononga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Patsala pangʼonongʼono kuti mkwiyo wanga uchoke pa inu ndipo ndidzaonetsa ukali wanga pa iwo mpaka kuwawononga.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti patsala kamphindi, ndipo ukali udzathedwa ndi mkwiyo wanga wakuwaononga.