Isaiah 10:6 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndikumtuma kwa mtundu wosasamala za Mulungu, ndipo ndikumlamula kuti apite kwa anthu amene ndaŵakwiyira, kuti akafunkhe ndi kukalanda chuma chao chonse, ndi kuŵaponderezera pansi ngati matope am'miseu.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ine ndidzamtumiza kumenyana ndi mtundu wosalemekeza, ndi pa anthu a mkwiyo wanga ndidzamlangiza, kuti afunkhe, agwire zolanda, awapondereze pansi, monga dothi la pamakwalala.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndidzamutuma kukalimbana ndi mtundu wosapembedza Mulungu, ndidzamutumiza kukalimbana ndi anthu amene amandikwiyitsa Ine, kukafunkha ndi kulanda chuma, ndi kuwapondereza pansi ngati matope a mʼmisewu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ine ndidzamtumiza kumenyana ndi mtundu wosalemekeza, ndi pa anthu a mkwiyo wanga ndidzamlangiza, kuti afunkhe, agwire zolanda, awapondereze pansi, monga dothi la pamakwalala.