Isaiah 13:16 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ana ao akhanda adzatswanyidwa iwo akuwona. M'nyumba mwao mudzafunkhidwa, ndipo akazi ao adzaŵachimwitsa mwakhakhamizo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Makanda ao adzatswanyidwe pamaso pao; m'nyumba mwao mudzafunkhidwa, ndi akazi ao adzakakamizidwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ana awo akhanda adzaphwanyidwa iwo akuona; nyumba zawo zidzafunkhidwa ndipo akazi awo adzagwiriridwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Makanda ao adzatswanyidwe pamaso pao; m'nyumba mwao mudzafunkhidwa, ndi akazi ao adzakakamizidwa.