Isaiah 14:16 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Anthu akufa akakuwona azidzakupenyetsetsa nkuyamba kulingalira za iwe kuti, ‘Kodi uyu si munthu uja ankanjenjemeretsa dziko lapansi, ndi kugwedeza maufumu?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Iwo amene akuona iwe adzayang'anitsitsa iwe, nadzalingalira za iwe, ndi kuti, Kodi uyu ndi munthu amene ananthunthumiritsa dziko lapansi, amene anagwedeza maufumu;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anthu akufa adzakupenyetsetsa nadzamalingalira za iwe nʼkumati, “Kodi uyu ndi munthu uja anagwedeza dziko lapansi ndi kunjenjemeretsa maufumu,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Iwo amene akuona iwe adzayang'anitsitsa iwe, nadzalingalira za iwe, ndi kuti, Kodi uyu ndi munthu amene ananthunthumiritsa dziko lapansi, amene anagwedeza maufumu;