Isaiah 14:20 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Sudzaikidwa nao m'manda mwaulemerero, chifukwa chakuti waononga dziko lako, wapha anthu ako. “Zidzukulu za anthu ochita zoipa zisadzakumbukike mpang'ono pomwe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Iwe sudzaphatikizidwa pamodzi nao poikidwa, pakuti iwe waononga dziko lako, wapha anthu ako; mbeu ya ochita zoipa sidzatchulidwa konse.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Sudzayikidwa nawo mʼmanda mwaulemu, chifukwa unawononga dziko lako ndi kupha anthu ako. Zidzukulu za anthu oyipa sizidzakumbukika nʼpangʼono pomwe.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Iwe sudzaphatikizidwa pamodzi nao poikidwa, pakuti iwe waononga dziko lako, wapha anthu ako; mbeu ya ocita zoipa sidzachulidwa konse.