Isaiah 14:26 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Zimenezi ndizo zimene ndagamula kuti zidzachitike pa dziko lonse lapansi. Ndatambalitsa dzanja langa kuti ndilange anthu a mitundu yonse.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Umenewu ndi uphungu wopangira dziko lonse; ndipo ili ndi dzanja lotambasulidwa pa amitundu onse.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Izi ndizo ndakonza kuti zichitike pa dziko lonse lapansi, ndatambasula dzanja pa anthu a mitundu yonse.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Umenewu ndi uphungu wopangira dziko lonse; ndipo ili ndi dzanja lotambasulidwa pa amitundu onse.